Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:24 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Benjamini anayang'anira Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Benjamini anayang'anira Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa fuko la Abenjamini anali Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abidani mwana wa Gideoni ndiye anali mtsogoleri wa mtundu wa Benjamini.

Onani mutuwo



Numeri 10:24
4 Mawu Ofanana  

Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Manase anayang'anira Gamaliele mwana wa Pedazuri.


Pamenepo anayenda a mbendera ya chigono cha ana a Dani, ndiwo a m'mbuyombuyo a zigono zonse, monga mwa magulu ao; ndi pa gulu lake anayang'anira Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Tsiku lachisanu ndi chinai kalonga wa ana a Benjamini, ndiye Abidani mwana wa Gideoni: