Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:15 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Isakara panali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Isakara panali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanele mwana wa Zuwara.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanieli mwana wa Zuwara,

Onani mutuwo



Numeri 10:15
4 Mawu Ofanana  

Wa Isakara, Netanele mwana wa Zuwara.


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndi gulu la fuko la ana a Zebuloni panali Eliyabu mwana wa Heloni.


Tsiku lachiwiri Netanele mwana wa Zuwara, kalonga wa Isakara, anabwera nacho chake: