Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:13 - Buku Lopatulika

Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kameneka kanali koyamba kuti Aisraele anyamuke, Chauta atalamula kudzera mwa Mose.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kameneka kanali koyamba kuti Aisraeli anyamuke monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo



Numeri 10:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo pokhala mtambo pamwamba pa chihema masiku pang'ono; pamenepo anakhala m'chigono monga awauza Yehova, nayendanso ulendo monga anauza Yehova.


Powauza Yehova amanga mahema, powauza Yehova ayenda ulendo; anasunga udikiro wa Yehova powauza Yehova mwa dzanja la Mose.


Yehova Mulungu wathu ananena ndi ife mu Horebu, ndi kuti Yakwanira nthawi yokhala inu m'phiri muno;