Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:25 - Buku Lopatulika

owerengedwa ao a fuko la Gadi, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

owerengedwa ao a fuko la Gadi, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Gadi, adapezeka kuti ali 45,650.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Gadi chinali 45, 650.

Onani mutuwo



Numeri 1:25
4 Mawu Ofanana  

A ana a Gadi, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


A ana a Yuda, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.


Iwo ndiwo mabanja a ana a Gadi, monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi anai ndi mazana asanu.