Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 8:7 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adamuuza kuti, “Chabwino, ndibwera kudzamchiritsa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yesu anati kwa iye, “Ine ndibwera kudzamuchiritsa.”

Onani mutuwo



Mateyu 8:7
5 Mawu Ofanana  

nati, Ambuye, mnyamata wanga ali gone m'nyumba wodwala manjenje, wozunzidwa koopsa.


Koma kenturiyoyo anavomera nati, Ambuye, sindiyenera kuti mukalowe pansi pa tsindwi langa iai; koma mungonena mau, ndipo adzachiritsidwa mnyamata wanga.


Ndipo Yesu anapita nao. Ndipo pakufika Iye tsono pafupi pa nyumba yake, kenturiyo anatuma kwa Iye abwenzi ake, kunena naye, Ambuye, musadzivute; pakuti sindiyenera ine kuti mudzalowe pansi pa tsindwi langa;