Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 7:10 - Buku Lopatulika

Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kapena atampempha nsomba, iye nkumupatsa njoka?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kapena ngati mwana apempha nsomba, kodi amamupatsa njoka?

Onani mutuwo



Mateyu 7:10
4 Mawu Ofanana  

Chomwecho, ngati inu, muli oipa, mudziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, kopambana kotani nanga Atate wanu wa Kumwamba adzapatsa zinthu zabwino kwa iwo akumpempha Iye?


Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?


Ndipo monga Mose anakweza njoka m'chipululu, chotero Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa;


Koma ndiopa, kuti pena, monga njoka inanyenga Heva ndi kuchenjerera kwake, maganizo anu angaipsidwe kusiyana nako kuona mtima ndi kuyera mtima zili kwa Khristu.