Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 7:1 - Buku Lopatulika

Musaweruze, kuti mungaweruzidwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musaweruze, kuti mungaweruzidwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Musamaweruza anthu ena kuti ndi olakwa, kuwopa kuti Mulungu angakuweruzeni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Musaweruze ena, kuti inunso mungadzaweruzidwe.

Onani mutuwo



Mateyu 7:1
13 Mawu Ofanana  

Imvani mau a Yehova, inu amene munthunthumira ndi mau ake; abale anu amene akudani inu, amene anaponya inu kunja chifukwa cha dzina langa, iwo anati, Yehova alemekezedwe, kuti ife tione kusangalala kwanu; koma iwo adzakhala ndi manyazi.


Pakuti ndi kuweruza kumene muweruza nako, inunso mudzaweruzidwa; ndipo ndi muyeso umene muyesa nao, kudzayesedwa kwa inunso.


Wonyenga iwe! Tayamba kuchotsa m'diso lako mtandawo, ndipo pomwepo udzapenyetsa kuchotsa kachitsotso m'diso la mbale wako.


Ndipo musawatsutsa, ndipo simudzamatsutsidwa. Khululukani, ndipo mudzakhululukidwa.


Ndipo uyang'aniranji kachitsotso kali m'diso la mbale wako, koma mtanda wa m'diso la iwe mwini suuzindikira?


Koma pamene anakhalakhala alikumfunsabe Iye, anaweramuka, nati kwa iwo, Amene mwa inu ali wopanda tchimo, ayambe kumponya mwala.


Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa.