Yakobo 3:1 - Buku Lopatulika1 Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Abale anga, musachuluke ofuna kukhala aphunzitsi, chifukwa monga mudziŵa, aphunzitsife tidzaweruzidwa mouma koposa anthu ena onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Abale anga, ambiri musakhale aphunzitsi chifukwa mumadziwa kuti aphunzitsife tidzaweruzidwa mowuma kuposa anthu ena onse. Onani mutuwo |