Yakobo 2:26 - Buku Lopatulika26 Pakuti monga thupi lopanda mzimu lili lakufa, koteronso chikhulupiriro chopanda ntchito chili chakufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pakuti monga thupi lopanda mzimu lili lakufa, koteronso chikhulupiriro chopanda ntchito chili chakufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Paja monga momwe thupi lopanda mzimu limakhala lakufa, moteronso chikhulupiriro chopanda ntchito zake nchakufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Monga thupi lopanda mzimu ndi lakufa, chomwechonso chikhulupiriro chopanda ntchito zabwino ndi chakufa. Onani mutuwo |