Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:6 - Buku Lopatulika

ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo otsala anagwira akapolo ake, nawachitira chipongwe, nawapha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Enawo adagwira antchito a mfumu aja naŵazunza, nkuŵapha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo otsalawo anagwira antchito ake, nawazunza ndi kuwapha.

Onani mutuwo



Mateyu 22:6
16 Mawu Ofanana  

Koma iwo ananyalanyaza, nachoka, wina kumunda wake, wina kumalonda ake:


Koma mfumu inakwiya; nituma asilikali ake napululutsa ambanda aja, nitentha mzinda wao.


Pakuti adzampereka kwa amitundu, nadzamseka, nadzamchitira chipongwe, nadzamthira malovu;


Ndipo Saulo analikuvomerezana nao pa imfa yake. Ndipo tsikulo kunayamba kuzunza kwakukulu pa Mpingo unali mu Yerusalemu; ndipo anabalalitsidwa onse m'maiko a Yudeya ndi Samariya, koma osati atumwi ai.


Kumbukirani am'nsinga, monga am'nsinga anzao; ochitidwa zoipa, monga ngati inunso adatero nanu m'thupi.