Luka 18:32 - Buku Lopatulika32 Pakuti adzampereka kwa amitundu, nadzamseka, nadzamchitira chipongwe, nadzamthira malovu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Pakuti adzampereka kwa amitundu, nadzamseka, nadzamchitira chipongwe, nadzamthira malovu; ndipo atamkwapula adzamupha Iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Akampereka kwa anthu akunja. Amenewo akamchita chipongwe, akamnyazitsa, ndi kumthira malovu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Iye adzaperekedwa kwa anthu a mitundu ina. Ndipo adzamuchita chipongwe, adzamunyoza, adzamulavulira, Onani mutuwo |