Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 2:21 - Buku Lopatulika

Ndipo anauka iye, natenga kamwana ndi amake, nalowa m'dziko la Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anauka iye, natenga kamwana ndi amake, nalowa m'dziko la Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Yosefe adanyamuka, nkutenga mwana uja ndi mai wake, kubwerera ku Israele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Yosefe atadzuka anatenga mwanayo ndi amayi ake kupita ku dziko la Israeli.

Onani mutuwo



Mateyu 2:21
4 Mawu Ofanana  

Chotero anachita Nowa, monga mwa zonse anamlamulira iye Mulungu, momwemo anachita.


nati, Tauka, nutenge kamwana ndi amake, nupite kudziko la Israele: chifukwa anafa uja wofuna moyo wake wa kamwanako.


Koma pakumva iye kuti Arkelao anali mfumu ya Yudeya m'malo mwa atate wake Herode, anachita mantha kupita kumeneko; ndipo pamene anachenjezedwa ndi Mulungu m'kulota, anamuka nalowa kudziko la Galileya,


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.