Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 16:5 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene ophunzira aja adakafika kutsidya, anali ataiŵala kutenga buledi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma atawoloka nyanja, ophunzira anayiwala kutenga buledi.

Onani mutuwo



Mateyu 16:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene Iye anauza makamuwo amuke, analowa m'ngalawa, nafika m'malire a Magadani.


Obadwa oipa ndi achigololo afunafuna chizindikiro; ndipo sadzalandira chizindikiro china, koma chizindikiro cha Yona. Ndipo Iye anawasiya, nachokapo.


Ndipo Yesu anati kwa iwo, Yang'anirani mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi ndi Asaduki.