Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:53 - Buku Lopatulika

Ndipo panali, pamene Yesu anatha mafanizo awa, anachokera kumeneko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali, pamene Yesu anatha mafanizo awa, anachokera kumeneko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu atatsiriza kunena mafanizoŵa, adachoka kumeneko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu atatsiriza mafanizowa anachoka kumeneko.

Onani mutuwo



Mateyu 13:53
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Chifukwa chake, mlembi aliyense, wophunzitsidwa mu Ufumu wa Kumwamba, ali wofanana ndi munthu mwini banja, amene atulutsa m'chuma chake zinthu zakale ndi zatsopano.


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake: