Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 12:6 - Buku Lopatulika

Koma ndinena kwa inu, kuti wakuposa Kachisiyo ali pompano.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ndinena kwa inu, kuti wakuposa Kachisiyo ali pompano.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipotu ndikunenetsa kuti pali wina pano woposa Nyumba ya Mulunguyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndikuwuzani kuti wamkulu kuposa Nyumba ya Mulunguyo ali pano.

Onani mutuwo



Mateyu 12:6
12 Mawu Ofanana  

Koma kodi nzoona kuti Mulungu akhala ndi anthu padziko lapansi? Taonani, thambo, inde m'mwambamwamba, sizifikira inu, koposa kotani nanga nyumba iyi ndaimanga?


Atero Yehova, Kumwamba ndi mpando wanga wachifumu, ndi dziko lapansi ndi choikapo mapazi anga; mudzandimangira Ine nyumba yotani? Ndi malo ondiyenera kupumamo ali kuti?


Pakuti zonsezi mkono wanga wazilenga, momwemo zonsezi zinaoneka, ati Yehova; koma ndidzayang'anira munthu uyu amene ali waumphawi, ndi wa mzimu wosweka, nanthunthumira ndi mau anga.


Taonani, ndituma mthenga wanga, kuti akonzeretu njira pamaso panga; ndipo Ambuye amene mumfuna adzadza ku Kachisi wake modzidzimutsa; ndiye mthenga wa chipangano amene mukondwera naye; taonani akudza, ati Yehova wa makamu.


Kapena simunawerenge kodi m'chilamulo, kuti tsiku la Sabata ansembe mu Kachisi amaipitsa tsiku la Sabata, nakhala opanda tchimo?


pakuti mwa Iye chikhalira chidzalo cha Umulungu m'thupi,