Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 10:9 - Buku Lopatulika

Musadzitengere ndalama zagolide, kapena zasiliva, kapena zakobiri m'malamba mwanu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musadzitengere ndalama zagolide, kapena zasiliva, kapena zakobiri m'malamba mwanu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musatenge ndalama m'zikwama, kaya nzagolide, kaya nzasiliva, kaya nzakopala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Musatenge ndalama zagolide kapena zasiliva kapena zakopala mʼzikwama mwanu;

Onani mutuwo



Mateyu 10:9
7 Mawu Ofanana  

Chiritsani akudwala, ukitsani akufa, konzani akhate, tulutsani ziwanda: munalandira kwaulere, patsani kwaulere.


Ndipo anadziitanira khumi ndi awiriwo, nayamba kuwatumiza iwo awiriawiri; nawapatsa mphamvu pa mizimu yonyansa;


Ndipo anati kwa iwo, Pamene ndinakutumizani opanda thumba la ndalama, ndi thumba la kamba, ndi nsapato, munasowa kanthu kodi? Anati iwo, Iai.