Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 81:4 - Buku Lopatulika

Pakuti ichi ndi cholemba cha kwa Israele, chiweruzo cha Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ichi ndi cholemba cha kwa Israele, chiweruzo cha Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pakuti ndilo lamulo lokhalira Israele, lochokera kwa Mulungu wa Yakobe,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ili ndi lamulo kwa Israeli, langizo la Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo



Masalimo 81:4
2 Mawu Ofanana  

Momwemo tsiku lakukondwera inu, ndi nyengo zoikidwa zanu, ndi poyamba miyezi yanu, muziliza malipenga pa nsembe zanu zopsereza, ndi pa nsembe zanu zoyamika; ndipo akhale kwa inu chikumbutso pamaso pa Mulungu wanu; Ine ndine Yehova Mulungu wanu.


Ndipo poyamba miyezi yanu muzibwera nayo nsembe yopsereza ya Yehova: ng'ombe zamphongo ziwiri, ndi nkhosa yamphongo imodzi, ndi anaankhosa asanu ndi awiri a chaka chimodzi opanda chilema;