Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 17:2 - Buku Lopatulika

Pankhope panu patuluke chiweruzo changa; maso anu apenyerere zolunjika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pankhope panu patuluke chiweruzo changa; maso anu apenyerere zolunjika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kusalakwa kwanga kuwonekere poyera pa chiweruzo chanu, maso anu aone kulungama kwanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu; maso anu aone chimene ndi cholungama.

Onani mutuwo



Masalimo 17:2
8 Mawu Ofanana  

Yehova sadzamsiya m'dzanja lake; ndipo sadzamtsutsa poweruzidwa iye.


Ndipo adzaonetsa chilungamo chako monga kuunika, ndi kuweruza kwako monga usana.


Koma mukuti, Njira ya Ambuye njosayenera. Tamvera tsono nyumba ya Israele, Kodi njira yanga njosayenera? Njira zanu si ndizo zosayenera?


Koma nyumba ya Israele imanena, Njira ya Ambuye njosayenera. Inu, nyumba ya Israele, kodi njira zanga nzosayenera? Njira zanu si ndizo zosayenera?


Koma ana a anthu a mtundu wako akuti, Njira ya Ambuye siiyenera; koma iwowa njira yao siiyenera.


Koma munati, Njira ya Ambuye siiyenera. Nyumba ya Israele inu, ndidzakuweruzani, yense monga mwa njira zake.


Ndipo kwa Iye amene akhoza kukudikirani mungakhumudwe, ndi kukuimikani pamaso pa ulemerero wake opanda chilema m'kukondwera,