Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 139:4 - Buku Lopatulika

Pakuti asanafike mau pa lilime langa, taonani, Yehova, muwadziwa onse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti asanafike mau pa lilime langa, taonani, Yehova, muwadziwa onse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngakhale mau anga asanafike pakamwa panga, Inu Chauta mumaŵadziŵa onse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mawu asanatuluke pa lilime langa mumawadziwa bwinobwino, Inu Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 139:4
13 Mawu Ofanana  

Ndani uyu adetsa uphungu, ndi mau opanda nzeru?


Ndani uyu abisa uphungu wosadziwa kanthu? Chifukwa chake ndinafotokozera zimene sindinazizindikire, zondidabwitsa, zosazidziwa ine.


Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti?


Mau a m'kamwa mwanga ndi maganizo a m'mtima wanga avomerezeke pamaso panu, Yehova, thanthwe langa, ndi Mombolo wanga.


chifukwa anachita zopusa mu Israele, nachita chigololo ndi akazi a anansi ao, nanena mau onama m'dzina langa, amene ndinawauza kuti asanene; Ine ndine wodziwa, ndi mboni, ati Yehova.


Ndipo kudzachitika nthawi yomweyi kuti ndidzasanthula Yerusalemu ndi nyali, ndipo ndidzalanga amunawo okhala ndi nsenga, onena m'mtima mwao, Yehova sachita chokoma, kapena kuchita choipa.


Ngati wina adziyesera ali wopembedza Mulungu, ndiye wosamanga lilime lake, koma adzinyenga mtima wake, kupembedza kwake kwa munthuyu nkopanda pake.