Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:16 - Buku Lopatulika

Pakamwa ali napo koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakamwa ali napo koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pakamwa ali napo, koma salankhula, maso ali nawo, koma sapenya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakamwa ali napo koma sayankhula maso ali nawo, koma sapenya;

Onani mutuwo



Masalimo 135:16
2 Mawu Ofanana  

Nenepetsa mtima wa anthu awa, lemeretsa makutu ao, nutseke maso ao; angaone ndi maso ao, angamve ndi makutu ao, angazindikire ndi mtima wao, nakabwerenso, nachiritsidwe.