Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:10 - Buku Lopatulika

Ndiye amene anapanda amitundu ambiri, napha mafumu amphamvu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndiye amene anapanda amitundu ambiri, napha mafumu amphamvu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye amene adaononga mitundu yambiri ya anthu, ndi kupha mafumu amphamvu aja,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anakantha mitundu yambiri ya anthu ndi kupha mafumu amphamvu:

Onani mutuwo



Masalimo 135:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anamkantha ndi lupanga lakuthwa, nalanda dziko lake likhale laolao, kuyambira Arinoni kufikira Yaboki, kufikira ana a Amoni; popeza malire a ana a Amoni ndiwo olimba.


Ndipo anamkantha iye, ndi ana ake aamuna ndi anthu ake onse, kufikira sanatsale ndi mmodzi yense; nalanda dziko lake likhale laolao.