Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 8:9 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu amene adaali pamenepo, amuna okha adaalipo ngati zikwi zinai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Panali amuna pafupifupi 4,000. Ndipo atawawuza kuti apite kwawo,

Onani mutuwo



Marko 8:9
4 Mawu Ofanana  

Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo pomwepo analowa m'ngalawa ndi ophunzira ake, nafika ku mbali ya ku Dalamanuta.


Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.


Ndipo anadzitengera khumi ndi awiriwo, nati kwa iwo, Taonani, tikwera kunka ku Yerusalemu, ndipo zidzakwaniritsidwa kwa Mwana wa Munthu zonse zolembedwa ndi aneneri.