Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 7:8 - Buku Lopatulika

Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka Yesu adati, “Inu mumasiya Malamulo a Mulungu, nkumasunga miyambo ya anthu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mwasiya malamulo a Mulungu ndipo mwagwiritsitsa miyambo ya anthu.”

Onani mutuwo



Marko 7:8
4 Mawu Ofanana  

Pakudzaonekera inu pamaso pa Ine, ndani wafuna chimenechi m'dzanja lanu, kupondaponda m'mabwalo mwanga?


Ndipo Afarisi ndi alembi anamfunsa Iye, kuti, Bwanji ophunzira anu satsata mwambo wa akulu, koma akudya mkate wao ndi m'manja mwakuda?


ndipo ndinawaposa ndi kutsogola mwa Chiyuda ambiri a msinkhu wanga mwa mtundu wanga, ndipo ndinakhala wachangu koposa pa miyambo ya makolo anga.