Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 5:1 - Buku Lopatulika

Ndipo anafika tsidya lina la nyanja, kudziko la Agerasa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anafika tsidya lina la nyanja, kudziko la Agerasa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu ndi ophunzira ake adafika ku tsidya la Nyanja ya Galileya, ku dera la Agerasa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anawoloka nyanja napita ku dera la Gerasa.

Onani mutuwo



Marko 5:1
4 Mawu Ofanana  

Ndipo dzuwa lomwelo, pofika madzulo, ananena kwa iwo, Tiolokere tsidya lina.


Ndipo iwo anachita mantha aakulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?