Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:3 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anayankha nati kwa iwo, Kodi Mose anakulamulani chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anayankha nati kwa iwo, Kodi Mose anakulamulani chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yesu poyankha adati, “Kodi Mose adakulamulani zotani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayankha kuti, “Kodi Mose anakulamulani chiyani?”

Onani mutuwo



Marko 10:3
6 Mawu Ofanana  

Kuchilamulo ndi kuumboni! Ngati iwo sanena malinga ndi mau awa, ndithu sadzaona mbandakucha.


Ndipo anadza kwa Iye Afarisi, namfunsa Iye ngati kuloledwa kuti munthu achotse mkazi wake, namuyesa Iye.


Ndipo anati, Mose analola kulembera kalata yachilekaniro, ndi kumchotsa.


Ndipo taonani, wachilamulo wina anaimirira namuyesa Iye, nanena, Mphunzitsi, ndidzalowa moyo wosatha ndi kuchita chiyani?


Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo;


Ndiuzeni, inu akufuna kukhala omvera lamulo, kodi simukumva chilamulo?