Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:1 - Buku Lopatulika

Ndipo chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa chinayandikira, ndicho chotchedwa Paska.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo phwando la mikate yopanda chotupitsa linayandikira, ndilo lotchedwa Paska.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi yochitira chikondwerero cha buledi wosafufumitsa inkayandikira. Chikondwererocho chimatchedwa Paska.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Phwando la buledi wopanda yisiti lotchedwa Paska litayandikira,

Onani mutuwo



Luka 22:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni m'dziko la Ejipito, ndi kuti,


Ndipo tsiku loyamba la mikate yopanda chotupitsa, pamene amapha Paska, ophunzira ananena naye, Mufuna tinke kuti, tikakonze mkadyereko Paska?


Koma pasanafike chikondwerero la Paska, Yesu, podziwa kuti nthawi yake idadza yakuchoka kutuluka m'dziko lino lapansi, kunka kwa Atate, m'mene anakonda ake a Iye yekha a m'dziko lapansi, anawakonda kufikira chimaliziro.