Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 21:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo anthu onse analawira mamawa kudza kwa Iye ku Kachisi kudzamvera Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo anthu onse analawira mamawa kudza kwa Iye ku Kachisi kudzamvera Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Tsono anthu onse ankalaŵirira m'mamaŵa kubwera kwa Iye ku Nyumba ya Mulungu kudzamva mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Ndipo anthu onse amabwera mmamawa kudzamumva Iye ku Nyumba ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:38
2 Mawu Ofanana  

Ndipo chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa chinayandikira, ndicho chotchedwa Paska.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa