Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 21:2 - Buku Lopatulika

Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaonanso mai wina wamasiye akuponyamo tindalama tiŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anaonanso mkazi wamasiye wosauka akuyikamo timakopala tiwiri.

Onani mutuwo



Luka 21:2
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.


Ndipo Iye anati, Zoonadi ndinena kwa inu, wamasiye uyu waumphawi anaikamo koposa onse;