Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Koma padafika mai wina wamasiye, wosauka. Iyeyu adangoponyamo tindalama tiŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Koma mkazi wamasiye, wosauka anabwera ndi kuyikamo tindalama tiwiri ta kopala, tongokwanira theka la ndalama.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:42
9 Mawu Ofanana  

Mwenzi utakhala ngati mlongo wanga, woyamwa pa bere la amai! Ndikadakupeza panja, ndikadakupsompsona; osandinyoza munthu.


Ndipo aliyense amene adzamwetsa mmodzi wa ang'ono awa chikho chokha cha madzi ozizira, pa dzina la wophunzira, indetu ndinena kwa inu, iye sadzataya mphotho yake.


Indetu ndinena ndi iwe, sudzatulukamo konse, koma utalipa kakobiri kakumaliza ndiko.


Ndipo Iye anakhala pansi pandunji pa mosungiramo ndalama, napenya kuti khamu la anthu alikuponya ndalama mosungiramo; ndipo eni chuma ambiri anaponyamo zambiri.


Ndipo anaitana ophunzira ake, nati kwa iwo, Ndithu ndinena ndi inu, Mkazi wamasiye amene waumphawi anaponya zambiri koposa onse akuponya mosungiramo:


Ine ndinena kwa iwe, Sudzatulukamo konse kufikira utalipira kakobiri kukumaliza.


Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.


Pakuti ngati chivomerezocho chili pomwepo, munthu alandiridwa monga momwe ali nacho, si monga chimsowa.


kuti m'chitsimikizo chachikulu cha chisautso, kuchulukitsa kwa chimwemwe chao, ndi kusauka kwao, kwenikweni zidachulukira ku cholemera cha kuolowa mtima kwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa