Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:6 - Buku Lopatulika

Ndipo panali pokhala iwo komweko, masiku ake a kubala anakwanira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali pokhala iwo komweko, masiku ake a kubala anakwanira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene anali kumeneko, nthaŵi yake yoti Maria achire idakwana,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ali kumeneko, nthawi inakwana yakuti mwana abadwe,

Onani mutuwo



Luka 2:6
7 Mawu Ofanana  

Chiweruzo cha Yehova chikhazikika chikhazikikire, zolingirira za m'mtima mwake ku mibadwomibadwo.


Muli zolingalira zambiri m'mtima mwa munthu; koma uphungu wa Yehova ndiwo udzaimika.


Koma iwe, Betelehemu Efurata, ndiwe wamng'ono kuti ukhale mwa zikwi za Yuda, mwa iwe mudzanditulukira wina wakudzakhala woweruza mu Israele; matulukiro ake ndiwo a kale lomwe, kuyambira nthawi yosayamba.


Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.


kukalembedwa iye mwini pamodzi ndi Maria, wopalidwa naye ubwenzi; ndi uyu anali ndi pakati.


Ndipo iye anabala mwana wake wamwamuna woyamba; namkulunga Iye m'nsalu, namgoneka modyera ng'ombe, chifukwa kuti anasowa malo m'nyumba ya alendo.