Masalimo 33:11 - Buku Lopatulika11 Chiweruzo cha Yehova chikhazikika chikhazikikire, zolingirira za m'mtima mwake ku mibadwomibadwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Chiweruzo cha Yehova chikhazikika chikhazikikire, zolingirira za m'mtima mwake ku mibadwomibadwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma zolinga za Chauta zimachitika nthaŵi zonse, maganizo a mumtima mwake amakhazikika mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma chikonzero cha Yehova chimakhala mpaka muyaya, zolinga za mu mtima mwake pa mibado yonse. Onani mutuwo |