Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:4 - Buku Lopatulika

kuti udziwitse zoona zake za mau amene unaphunzira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kuti udziwitse zoona zake za mau amene unaphunzira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndatero kuti mudziŵe ndithu kuti zimene adakuphunzitsanizo nzoonadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuti mudziwe bwinobwino zoona za zinthu zimene mwaphunzitsidwa.

Onani mutuwo



Luka 1:4
7 Mawu Ofanana  

kuti ukadziwitse ntheradi yake ya mau oona, nukabwere ndi mau oona kwa iwo amene anakutumiza?


koma zalembedwa izi kuti mukakhulupirire kuti Yesu ndiye Khristu Mwana wa Mulungu, ndi kuti pakukhulupirira mukhale nao moyo m'dzina lake.


Iyeyo anaphunzitsidwa m'njira ya Ambuye; pokhala nao mzimu wachangu, ananena ndi kuphunzitsa mosamalira zinthu za Yesu, ndiye wodziwa ubatizo wa Yohane wokha;


nudziwa chifuniro chake, nuvomereza zinthu zoposa, utaphunzitsidwa m'chilamulo,


koma mu Mpingo ndifuna kulankhula mau asanu ndi zidziwitso changa, kutinso ndikalangize ena, koposa kulankhula mau zikwi m'lilime.


Koma iye amene aphunzira mau, ayenera kuchereza womphunzitsayo m'zonse zabwino.