Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:19 - Buku Lopatulika

19 koma mu Mpingo ndifuna kulankhula mau asanu ndi zidziwitso changa, kutinso ndikalangize ena, koposa kulankhula mau zikwi m'lilime.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 koma mu Mpingo ndifuna kulankhula mau asanu ndi zidziwitso changa, kutinso ndikalangize ena, koposa kulankhula mau zikwi m'lilime.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Komabe mu msonkhano wa mpingo, m'malo molankhula mau ochuluka m'chilankhulo chosadziŵika, ndingakonde kwambiri kunena mau asanu okha omveka bwino, kuti ndiphunzitsire anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Koma mu mpingo ndi kwabwino kuti ndiyankhule mawu asanu okha omveka bwino kuti ndilangize bwino ena kusiyana ndikuyankhula mawu ambirimbiri mʼmalilime.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:19
5 Mawu Ofanana  

kuti udziwitse zoona zake za mau amene unaphunzira.


Ndiyamika Mulungu kuti ndilankhula malilime koposa inu nonse;


Abale, musakhale ana m'chidziwitso, koma m'choipa khalani makanda, koma m'chidziwitso akulu misinkhu.


Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa