Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 9:8 - Buku Lopatulika

Ndipo Mulungu ananena kwa Nowa ndi kwa ana ake pamodzi naye, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mulungu ananena kwa Nowa ndi kwa ana ake pamodzi naye, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu adauza Nowa ndi ana ake kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mulungu anawuza Nowa ndi ana ake kuti,

Onani mutuwo



Genesis 9:8
3 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo Yehova anapangana chipangano ndi Abramu, nati, Ndidzapatsa mbeu zako dziko ili, kuyambira pamtsinje wa ku Ejipito kufikira pamtsinje waukulu, mtsinje wa Yufurate:


Ndi inu, mubalane, muchuluke; muswane padziko lapansi, nimuchuluke m'menemo.


Ndipo Ine, taonani, Ine ndikhazikitsa pangano langa pamodzi ndi inu, ndi mbeu zanu pambuyo panu;