Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 7:19 - Buku Lopatulika

Ndipo madzi anapambana ndithu padziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pathambo lonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo madzi anapambana ndithu pa dziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pa thambo lonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kukwera kwa madzi kudapitirira ndithu mpaka kumiza ndi mapiri aatali omwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Madzi a chigumula anabwerabe molimbika motero kuti mapiri ataliatali onse a pa dziko anamizidwa.

Onani mutuwo



Genesis 7:19
7 Mawu Ofanana  

Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu padziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi.


Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri.


Taona atsekera madzi, naphwa; awatsegulira, ndipo akokolola dziko lapansi.


Ndithu akhulupirira mwachabe chithandizo cha kuzitunda, ndi phokoso la kumapiri; ndithu mwa Yehova Mulungu wathu muli chipulumutso cha Israele.


mwa izi dziko lapansi la masiku aja, pomizika ndi madzi, lidaonongeka;