Genesis 7:20 - Buku Lopatulika20 Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsono adakwererakwerera ndithu mpaka kubzola nsonga za mapiriwo mamita asanu ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Madzi anakwera namiza mapiri kwa mamita pafupifupi asanu ndi awiri. Onani mutuwo |