Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 7:20 - Buku Lopatulika

20 Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsono adakwererakwerera ndithu mpaka kubzola nsonga za mapiriwo mamita asanu ndi aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Madzi anakwera namiza mapiri kwa mamita pafupifupi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 7:20
5 Mawu Ofanana  

Kupanga kwake ndi kotere: m'litali mwake mwa chingalawa mikono mazana atatu, m'mimba mwake mikono makumi asanu, m'msinkhu mwake mikono makumi atatu.


Ndipo madzi anapambana ndithu padziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pathambo lonse.


Ndipo chingalawa chinaima pamapiri a Ararati, mwezi wachisanu ndi chiwiri, tsiku lakhumi ndi asanu ndi awiri la mwezi.


Mudalikuta ndi nyanja ngati ndi chovala; madzi anafikira pamwamba pa mapiri.


Ndithu akhulupirira mwachabe chithandizo cha kuzitunda, ndi phokoso la kumapiri; ndithu mwa Yehova Mulungu wathu muli chipulumutso cha Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa