2 Petro 3:6 - Buku Lopatulika6 mwa izi dziko lapansi la masiku aja, pomizika ndi madzi, lidaonongeka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 mwa izi dziko lapansi la masiku aja, pomizika ndi madzi, lidaonongeka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo ndi madzi okhaokhawo dziko lapansi la masiku amenewo lidamizidwa ndi kuwonongedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndi madzinso achigumula, dziko lapansi la masiku amenewo linawonongedwa. Onani mutuwo |