Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:8 - Buku Lopatulika

masiku ake onse a Seti anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi ndi ziwiri; ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

masiku ake onse a Seti anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi ndi ziwiri; ndipo anamwalira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adamwalira ali wa zaka 912.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.

Onani mutuwo



Genesis 5:8
3 Mawu Ofanana  

Masiku ake onse anakhala ndi moyo Adamu anali zaka mazana asanu ndi anai, kudza makumi atatu; ndipo anamwalira.


ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:


Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;