Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:7 - Buku Lopatulika

ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo adakhalanso ndi moyo zaka zina 807. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo



Genesis 5:7
4 Mawu Ofanana  

Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi;


masiku ake onse a Seti anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi ndi ziwiri; ndipo anamwalira.


mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.