Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 41:9 - Buku Lopatulika

Pamenepo wopereka chikho wamkulu anati kwa Farao, kuti, Ine ndidzakumbukira zochimwa zanga lero.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo wopereka chikho wamkulu anati kwa Farao, kuti, Ine ndidzakumbukira zochimwa zanga lero.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pomwepo woperekera vinyo uja adauza Farao kuti, “Lero ndiwulule kulakwa kwanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mkulu wa operekera zakumwa anati kwa Farao, “Lero ndakumbukira kulephera kwanga.

Onani mutuwo



Genesis 41:9
4 Mawu Ofanana  

Koma undikumbukire ine m'mene kudzakhala bwino ndi iwe, ndipo undichitiretu ine kukoma mtima: nunditchule ine kwa Farao, nunditulutse ine m'nyumbamu:


Koma wopereka chikho wamkulu sanakumbukire Yosefe, koma anamuiwala.


kufikira nyengo yakuchitika maneno ake; mau a Yehova anamuyesa.