Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:3 - Buku Lopatulika

Tsopano tengatu zida zako ndi phodo lako ndi uta wako, numuke kuthengo kundisakira ine nyama:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsopano tengatu zida zako ndi phodo lako ndi uta wako, numuke kuthengo kundisakira ine nyama:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tenga zida zako, uta ndi mivi yomwe, upite ku thengo ukandiphere nyama.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono tenga zida zako, muvi wako ndi uta, pita kuthengo ukandiphere nyama.

Onani mutuwo



Genesis 27:3
5 Mawu Ofanana  

Iye ndiye mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova: chifukwa chake kunanenedwa, Monga Nimirodi mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova.


nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.


Munthu adzafikako ndi mivi ndi uta; pakuti dziko lonse lidzakhala la lunguzi ndi minga.


Zinthu zonse ziloledwa kwa ine; koma si zonse zipindula. Zinthu zonse ziloledwa kwa ine, koma sindidzalamulidwa nacho chimodzi.