Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 27:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Tsono tenga zida zako, muvi wako ndi uta, pita kuthengo ukandiphere nyama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Tsopano tengatu zida zako ndi phodo lako ndi uta wako, numuke kuthengo kundisakira ine nyama:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Tsopano tengatu zida zako ndi phodo lako ndi uta wako, numuke kuthengo kundisakira ine nyama:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Tenga zida zako, uta ndi mivi yomwe, upite ku thengo ukandiphere nyama.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:3
5 Mawu Ofanana  

Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”


Undikonzere chakudya chabwino monga muja ndimakonderamu ndipo ubwere nacho kwa ine kuti ndidye ndi kuti ndikudalitse ndisanamwalire.”


Anthu adzapita kumeneko kukachita uzimba ali ndi uta ndi mivi, popeza kuti mʼdziko monsemo mudzakhala mkandankhuku ndi minga.


Inu mumati, “Ine ndili ndi ufulu wochita chilichonse.” Komatu si zonse zimene nʼzothandiza. “Ndili ndi ufulu wochita chilichonse.” Koma sindidzagonjetsedwa ndi chilichonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa