Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:16 - Buku Lopatulika

ndi Ayebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Ayebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ameneŵa adabereka Ayebusi, Aamori, Agirigasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ayebusi, Aamori, Agirigasi;

Onani mutuwo



Genesis 10:16
9 Mawu Ofanana  

ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini;


Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe.


Akeni ndi Akenizi, Akadimoni,


ndi Aamori, ndi Akanani, ndi Agirigasi, ndi Ayebusi.


Ndipo Gadi anafika tsiku lomwelo kwa Davide nanena naye, Kwerani mukamangire Yehova guwa la nsembe pa dwale la Arauna Myebusi.


ndi Ayebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi,


Ndipo ndidzachotsa mwazi wake m'kamwa mwake, ndi zonyansa zake pakati pa mano ake; momwemo iyenso adzakhala wotsalira wa Mulungu wathu, ndipo adzakhala ngati mkulu wa fuko mu Yuda, ndi Ekeroni ngati Myebusi.


Pamene Yehova Mulungu wanu atakulowetsani m'dziko limene munkako kulilandira likhale lanulanu, ndipo atakataya amitundu ambiri pamaso panu, Ahiti, ndi Agirigasi, ndi Aamori, ndi Akanani, ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi, mitundu isanu ndi iwiri yaikulu ndi yamphamvu yoposa inu;


Koma ana a Benjamini sanaingitse Ayebusi okhala mu Yerusalemu; koma Ayebusi anakhala mu Yerusalemu pamodzi ndi ana a Benjamini, mpaka lero lino.