Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:13 - Buku Lopatulika

Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ejipito ndi amene anali kholo la anthu a ku Ludi, Anamu, Lehabu, Nafutu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,

Onani mutuwo



Genesis 10:13
5 Mawu Ofanana  

ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mzinda waukulu.


Ndi ana aamuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani.


Kwerani, inu akavalo; chitani misala, inu magaleta, atuluke amphamvu; Akusi ndi Aputi, ogwira chikopa; ndi Aludi, amene agwira ndi kukoka uta.


Kusi, ndi Puti, ndi Ludi, ndi osokonezeka onse, ndi Libiya, ndi anthu a dziko lopangana nao, adzagwa pamodzi nao ndi lupanga.