Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 1:13 - Buku Lopatulika

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachitatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachitatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo kudali madzulo ndiponso m'maŵa, tsiku lachitatu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo panali madzulo ndiponso mmawa pa tsiku lachitatu.

Onani mutuwo



Genesis 1:13
6 Mawu Ofanana  

Ndipo dziko lapansi linamera udzu, therere lobala mbeu monga mwa mtundu wake, ndi mtengo wakubala zipatso, momwemo muli mbeu yake, monga mwa mtundu wake; ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.


Ndipo Mulungu anati, Pakhale zounikira pathambo la kumwamba, zakulekanitsa usana ndi usiku; zikhale zizindikiro ndi nyengo, ndi masiku, ndi zaka;


Ndipo anaziona Mulungu zonse zimene adazipanga, ndipo, taonani, zinali zabwino ndithu. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu ndi chimodzi.


Ndipo Mulungu anatcha kuyerako Usana, ndi mdimawo anautcha Usiku. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku loyamba.


Ndipo Mulungu analitcha thambolo Kumwamba. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachiwiri.


Ndipo Yesu ananena naye, Ndithu ndinena ndi iwe, kuti lero, usiku uno, tambala asanalire kawiri, udzandikana Ine katatu.