Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Filemoni 1:18 - Buku Lopatulika

Koma ngati anakulakwira kanthu, kapena wokongola kanthu, kanthu, kapena wakongola kanthu, undiwerengere ine kameneko;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati anakulakwira kanthu, kapena wokongola kanthu, kanthu, kapena wakongola kanthu, undiwerengere ine kameneko;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngati adakulakwirapo, kapena ali ndi ngongole kwa iwe, ngongoleyo ikhale yanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati anakulakwira kapena kukongola kanthu kalikonse, ndidzalipira ineyo.

Onani mutuwo



Filemoni 1:18
4 Mawu Ofanana  

Ine ndidzakhala chikole, pa manja anga mudzamfunsa: ndikapanda kumbwezera kwa inu ndi kumuimitsa pamaso panu, chifukwa chake chidzakhala pa ine masiku onse:


Ngati tsono undiyesa woyanjana nawe, umlandire iye monga ine mwini.


ine Paulo ndichilemba ndi dzanja langa, ndidzachibwezera ine; kuti ndisanene nawe kuti iwe ndiwe mangawa anga.