Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 9:21 - Buku Lopatulika

koma iyeyu wosasamalira mau a Yehova anasiya anyamata ndi zoweta zake kubusa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma iyeyu wosasamalira mau a Yehova anasiya anyamata ndi zoweta zake kubusa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe ena sadasamaleko zimene Chauta adanenazo, ndipo adangosiya panja akapolo ao pamodzi ndi zoŵeta zomwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iwo amene ananyozera mawu a Yehova anasiya akapolo ndi ziweto zawo panja.

Onani mutuwo



Eksodo 9:21
11 Mawu Ofanana  

Perekani tsono mtima ndi moyo wanu kufunafuna Yehova Mulungu wanu; ndipo nyamukani ndi kumanga malo opatulika a Yehova Mulungu, kuti abwere nalo likasa la chipangano la Yehova, ndi zipangizo zopatulika za Mulungu, kunyumba imene idzamangidwira dzina la Yehova.


Akadzikumbukira yekha mumtima mwake, akadzisonkhanitsira yekha mzimu wake ndi mpweya wake,


Munthu ndani kuti mumkuze, ndi kuti muike mtima wanu pa iye,


Ndipo Farao anatembenuka, nalowa m'nyumba yake, osasamalira ichi chomwe mumtima mwake.


Iyeyu wa anyamata a Farao wakuopa mau a Yehova anathawitsira m'zinyumba anyamata ake ndi zoweta zake;


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasula dzanja lako kuthambo, kuti pakhale matalala padziko lonse la Ejipito, pa anthu ndi pa zoweta, ndi pa zitsamba zonse zakuthengo, m'dziko la Ejipito.


Wochenjera aona zoipa, nabisala; koma achibwana angopitirira, nalipitsidwa.


Pamenepo ndinayang'ana ndi kuganizira, ndinaona ndi kulandira mwambo.


Ndipo munthuyu anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, penya ndi maso ako, imva m'makutu mwako, nuike mtima wako pa zonse ndidzakuonetsa iwe; pakuti unatengedwa kudza kuno, kuti ndikuonetse izi; fotokozera nyumba ya Israele zonse uziona.


Pamenepo anati kwa ine, Usaope Daniele; pakuti kuyambira tsiku loyamba lija unaika mtima wako kuzindikira ndi kudzichepetsa pamaso pa Mulungu wako, mau ako anamveka; ndipo ndadzera mau ako.


Ndipo pamene adati amwalire, anthu aakazi akukhala naye ananena, Usaope, popeza waona mwana wamwamuna. Koma iye sanayankhe, kapena kusamalira.