Eksodo 9:21 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Koma iwo amene ananyozera mawu a Yehova anasiya akapolo ndi ziweto zawo panja. Onani mutuwoBuku Lopatulika21 koma iyeyu wosasamalira mau a Yehova anasiya anyamata ndi zoweta zake kubusa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 koma iyeyu wosasamalira mau a Yehova anasiya anyamata ndi zoweta zake kubusa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Komabe ena sadasamaleko zimene Chauta adanenazo, ndipo adangosiya panja akapolo ao pamodzi ndi zoŵeta zomwe. Onani mutuwo |