Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 8:30 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose atachoka kwa Faraoko, adakapemphera kwa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Mose anasiyana ndi Farao nakapemphera kwa Yehova.

Onani mutuwo



Eksodo 8:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.


Ndipo Mose ndi Aroni anatuluka kwa Farao; ndi Mose anafuulira kwa Yehova kunena za achule amene adawaika pa Farao.


Ndipo Yehova anachita monga mwa mau a Mose; nachotsera Farao ndi anyamata ake ndi anthu ake mizazayo, sunatsale ndi umodzi wonse.


Ndipo Mose anatuluka kwa Farao m'mzinda nakweza manja ake kwa Yehova; ndipo mabingu ndi matalala analeka, ndi mvula siinavumbanso padziko.


Chifukwa chake muvomerezane wina ndi mnzake machimo anu, ndipo mupempherere wina kwa mnzake kuti muchiritsidwe. Pemphero la munthu wolungama likhoza kwakukulu m'machitidwe ake.