Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 6:28 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali, tsiku limene Yehova ananena ndi Mose m'dziko la Ejipito,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali, tsiku limene Yehova ananena ndi Mose m'dziko la Ejipito,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Chauta adalankhula ndi Mose ku dziko la Ejipito,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano pamene Yehova anayankhula kwa Mose mu Igupto,

Onani mutuwo



Eksodo 6:28
2 Mawu Ofanana  

Awa ndi omwewo ananena ndi Farao, mfumu ya Aejipito, awatulutse ana a Israele mu Ejipito; Mose ndi Aroni amenewa.


Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti, Ine ndine Yehova; lankhula ndi Farao mfumu ya Aejipito zonsezi Ine ndizinena nawe.